Matthew 9:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo aphunzitsi ena a Malamulo adayamba kudzifunsa mumtima mwao kuti, “Munthu ameneyu akuchita chipongwe Mulungu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu achitira Mulungu mwano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamenepo aphunzitsi ena amalamulo anaganiza mu mtima mwawo kuti, “Munthu uyu akuchitira Mulungu mwano.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu acitira Mulungu mwano.