Micah 1:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Chauta akuti, “Samariyayo ndidzamsandutsa bwinja, malo olimamo munda wamphesa. Miyala yake ndidzaitaya ku zigwa, ndipo maziko ake ndidzaŵafukula.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ndidzaika Samariya ngati mulu wa miyala ya m'munda, ngati zooka m'munda wamphesa; ndipo ndidzataya miyala yake m'chigwa, ndi kufukula maziko ake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja, malo odzalamo mphesa. Miyala yake ndidzayitaya ku chigwa ndipo ndidzafukula maziko ake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ndidzaika Samariya ngati mulu wa miyala ya m'munda, ngati zooka m'munda wamphesa; ndipo ndidzataya miyala yace m'cigwa, ndi kufukula maziko ace.