Micah 2:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono pa nthaŵi imene Chauta adzabwezeranso dziko kwa anthu ake, inuyo simudzalandirako gawo lililonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake udzasowa woponya chingwe chamaere m'msonkhano wa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova kuti agawe dziko pochita maere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace udzasowa woponya cingwe camaere m'msonkhano wa Yehova.