Micah 2:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu amandiwuza kuti, “Musatilalikire, munthu asalalike zimenezi. Manyazi sadzatigwera ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musamanenera, amanenera ati. Sadzanenera kwa awa; matonzo sadzachoka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aneneri awo amanena kuti, “Usanenere! Usanenere ndi pangʼono pomwe zimenezi; ife sitidzachititsidwa manyazi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musamanenera, amanenera ati. Sadzanenera kwa awa; matonzo sadzacoka.