Micah 2:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Monga zoterezi nzoyenera kuzinena, inu a banja la Yakobe? Kodi kuleza mtima kwa Chauta kwatheratu? Kodi zimenezi nzimene adachita? Kodi mau ake sadzetsa zabwino kwa munthu woyenda molungama?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? Izi ndi ntchito zake kodi? Mau anga samchitira zokoma kodi, iye amene ayenda choongoka?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena: “Kodi Mzimu wa Yehova wakwiya? Kodi Iye amachita zinthu zotere?” “Kodi mawu ake sabweretsa zabwino kwa amene amayenda molungama?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi adzati, Nyumba ya Yakobo iwe, Mzimu wa Yehova waperewera kodi? izi ndi nchito zace kodi? Mau anga samcitira zokoma kodi, iye amene ayenda coongoka?