Micah 2:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akazi a anthu anga mumaŵatulutsa m'nyumba zao zokoma. Ndipo ana ao mumaŵalanda madalitso anga kosalekeza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muwataya akazi a anthu anga kunja kwa nyumba zao zokondweretsa; muchotsa ulemerero wanga kwa ana ao kosatha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mumatulutsa akazi a anthu anga mʼnyumba zawo zabwino. Mumalanda ana awo madalitso anga kosatha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muwataya akazi a anthu anga kunja kwa nyumba zao zokondweretsa; mucotsa ulemerero wanga kwa ana ao kosatha.