Micah 3:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Imvani izi inu atsogoleri a banja la Yakobe, inu olamulira a banja la Israele. Inu mumadana ndi chilungamo, mumakhotetsa zinthu zokhoza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tamvanitu ichi, akulu a nyumba ya Yakobo inu, ndi oweruza a nyumba ya Israele inu, akuipidwa nacho chiweruzo, ndi kupotoza zoongoka zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Imvani izi, inu atsogoleri a nyumba ya Yakobo, inu olamulira nyumba ya Israeli, inu amene mumadana ndi kuweruza kolungama; ndipo mumakhotetsa zinthu zonse zolondola;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tamvanitu ici, akuru a nyumba ya Yakobo inu, ndi oweruza a nyumba ya Israyeli inu, akuipidwa naco ciweruzo, ndi kupotoza zoongoka zonse.