Micah 5:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komabe Chauta akuuza Aisraele kuti, “Pa tsiku limenelo ndidzaononga akavalo anu onse, ndipo ndidzaphwasula magaleta anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzachitika tsiku ilo, ati Yehova, ndidzaononga akavalo ako m'kati mwako, ndi kutha magaleta ako;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova akuti, “Tsiku limenelo ndidzawononga akavalo anu onse ndi kuphwasula magaleta anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzacitika tsiku ilo, ati Yehova, ndidzaononga akavalo ako m'kati mwako, ndi kutha magareta ako;