Micah 5:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzaononga mizinda ya m'dziko mwanu ndi kugwetseratu malinga anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo ndidzaononga midzi ya m'dziko lako, ndi kupasula malinga ako onse;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzawononga mizinda ya mʼdziko mwanu ndi kugwetsa malinga anu onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo ndidzaononga midzi ya m'dziko lako, ndi kupasula malinga ako onse;