Micah 6:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mudzadya, koma simudzakhuta. Njala sidzakuchokani. Mudzakundika zinthu, koma sizidzasungika. Zimene mudzakundika zidzaonongedwa pa nkhondo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzachotsa koma osalanditsa; ndi ichi wachilanditsa ndidzachipereka kulupanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mudzadya, koma simudzakhuta; mudzakhalabe ndi njala. Mudzasunga zinthu, koma sizidzasungika, chifukwa zimene mudzasunga zidzawonongedwa ndi lupanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzacotsa koma osalanditsa; ndi ici wacilanditsa ndidzacipereka kulupanga.