Nahum 3:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mutungiretu madzi kuti adzakwanire pa nthaŵi yokuzingani, limbitsani malinga anu. Pondani dothi, ponyani m'chikombole, ndipo muumbe njerwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Udzitungiretu madzi a nthawi yokumangira misasa, limbikitsa malinga ako, lowa kuthope, ponda dothi, limbitsa ng'anjo yanjerwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tungani madzi woti mudzamwe nthawi ya kuzunguliridwa kwanu, limbitsani chitetezo chanu! Pondani dothi, ikani mʼchikombole, konzani khoma la njerwa!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Udzitungiretu madzi a nthawi yokumangira misasa, limbikitsa malinga ako, lowa kuthope, ponda dothi, limbitsa ng'anjo yanjerwa.