Nahum 3:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Imvani kulira kwa zikoti, kukokoma kwa mikombero, likitilikiti wa akavalo ndi kulilima kwa magaleta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kumveka kwa chikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magaleta; ndi kaphatakaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magaleta;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kulira kwa zikwapu, mkokomo wa mikombero, kufuwula kwa akavalo ndiponso phokoso la magaleta!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kumveka kwa cikoti, ndi mkokomo wa kuyenda kwa njinga za magareta; ndi kaphata kaphata wa akavalo, ndi gwegwegwe wa magareta;