Nehemiah 12:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wa fuko la Salai anali Kalai, wa fuko la Amoki anali Eberi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
wa fuko la Salai anali Kalai; wa fuko la Amoki anali Eberi;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
wa Salai, Kalai; wa Amoki, Eberi;