Nehemiah 5:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine nditamva madandaulo amenewo, ndidapsa mtima kwambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pakumva kulira kwao, ndi mau ao, kunandiipira kwambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nditamva madandawulo awo ndi zimene amanenazi ndinapsa mtima kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pakumva kulira kwao, ndi mau ao, kunandiipira kwambiri.