Nehemiah 7:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amuna a ku Rama ndi Geba, 621.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a ku Rama ndi Geba — 621
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.