Nehemiah 7:62 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
A banja la Delaya, a banja la Tobiya, a banja la Nekoda 642.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda — 642.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.