Nehemiah 7:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
A banja la Parosi 2,172.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zidzukulu za Parosi — 2,172
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ana a Parosi zikwi ziwiri mphambu zana limodzi kudza makumi asanu ndi awiri.