Numbers 10:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kameneka kanali koyamba kuti Aisraele anyamuke, Chauta atalamula kudzera mwa Mose.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kameneka kanali koyamba kuti Aisraeli anyamuke monga momwe Yehova analamulira Mose.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.