Numbers 10:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma iye adayankha kuti, “Sindipita nao, ndipita kwathu kwa abale anga.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma anati kwa iye, Sindidzamuka nanu; koma ndipita ku dziko langa, ndi kwa abale anga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Hobabu anayankha kuti, “Ayi, sindipita nanu, ndibwerera ku dziko la kwathu ndi kwa abale anga.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma anati kwa iye, Sindidzamuka nanu; koma ndipita ku dziko langa, ndi kwa abale anga.