Numbers 10:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene mpingo wonse uyenera kusonkhana pamodzi, mulize lipenga, koma musalize lipenga lochenjeza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pofuna kusonkhanitsa anthu, muziliza malipenga, koma mosiyana ndi mmene malipenga ochenjeza amalizidwira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pomemeza msonkhano mulize, wosati cokweza ai.
Recommended Reading