Numbers 11:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ine sindingathe kuŵasamala ndekha anthu onseŵa. Katundu ameneyu sindingathe kumsenza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Sinditha kuwasenza anthu awa onse ndekha, pakuti andilemera ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sindingathe kusamala anthu onsewa ndekha. Katundu ameneyu ndi wolemera kwambiri kwa ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Sinditha kuwasenza anthu awa onse ndekha, pakuti andilemera ine.