Numbers 12:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Mose anali munthu wofatsa kupambana anthu onse a pa dziko lapansi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munthuyu Mose ndiye wofatsa woposa anthu onse a pa dziko lapansi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Koma Mose anali munthu wodzichepetsa kwambiri kuposa munthu aliyense pa dziko lapansi).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munthuyu Mose ndiye wofatsa woposa anthu onse a pa dziko lapansi.