Numbers 12:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma sinditero ndi mtumiki wanga Mose, amene wakhala woyang'anira anthu anga onse a Israeli.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Satero mtumiki wanga Mose; ndiye wokhulupirika m'nyumba mwanga monse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma sinditero ndi Mose mtumiki wanga; Iyeyu ndi wokhulupirika mʼnyumba yanga yonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Satero mtumiki wanga Mose; ndiye wokhulupirika m'nyumba mwanga monse.