Numbers 13:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'fuko la Yosefe (ndiye kuti m'fuko la Manase) adatuma Gadi mwana wa Susi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wa fuko la Yosefe, wa fuko la Manase, Gadi mwana wa Susi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuchokera ku fuko la Manase (fuko la Yosefe), Gadi mwana wa Susi;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wa pfuko la Yosefe, wa pfuko la Manase, Gadi mwana wa Susi.