Numbers 13:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'fuko la Dani, adatuma Amiyele mwana wa Gemali.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wa fuko la Dani, Amiyele mwana wa Gemali.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuchokera ku fuko la Dani, Amieli mwana wa Gemali;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wa pfuko la Dani, Amiyeli mwana wa Gemali.