Numbers 13:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'fuko la Nafutali, adatuma Nabi mwana wa Vofusi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wa fuko la Nafutali, Nabi mwana wa Vofusi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuchokera ku fuko la Nafutali, Naabi mwana wa Vofisi;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wa pfuko la Nafitali, Nabi mwana wa Vopisi.