Numbers 13:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patapita masiku makumi anai, anthu aja adabwerako kumene adakazonda dziko kuja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo anabwerera atazonda dziko, atatha masiku makumi anai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita masiku makumi anayi, anthu aja anabwerako kokazonda dziko lija.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo anabwerera atazonda dziko, atatha masiku makumi anai.