Numbers 13:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maina ao ndi aŵa: m'fuko la Rubeni, adatuma Samuwa mwana wa Zakuri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maina ao ndi awa: wa fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mayina awo ndi awa: kuchokera ku fuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maina ao ndi awa: wa pfuko la Rubeni, Samuwa mwana wa Zakuri.