Numbers 13:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
M'fuko la Yuda, adatuma Kalebe mwana wa Yefune.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuchokera ku fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune;
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wa pfuko la Yuda, Kalebi mwana wa Yefune.