Numbers 14:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsopano mukaŵapha onse anthu ameneŵa, mitundu ina imene yamva mbiri yanu idzati,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mukapha anthu awa ngati munthu mmodzi, pamenepo amitundu amene adamva mbiri yanu adzanena, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono mukawapha anthu onsewa nthawi imodzi, mayiko amene anamva za Inu adzati,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mukapha anthu awa ngati munthu mmodzi, pamenepo amitundu amene adamva mbiri yanu adzanena, ndi kuti,