Numbers 14:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ndikukupemphani, Chauta muwonetse kuti mphamvu zanu nzazikulu monga mudalonjezera kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo tsopano, ikuletu mphamvu ya Mbuye wanga, monga mudanena, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Chonde Ambuye wonetsani mphamvu yanu monga munalonjezera kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo tsopano, ikuletu mphamvu ya Mbuye wanga, monga mudanena, ndi kuti,