Numbers 14:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adati, “Ndaŵakhululukira chifukwa cha mau ako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova anati, Ndakhululukira monga mwa mau ako:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anayankha kuti, “Ndawakhululukira monga wapemphera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova anati, Ndakhululukira monga mwa mau ako: