Numbers 14:37 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu onsewo amene ankasimba zoipa za dzikolo, adafa ndi mliri pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu amene ankafalitsa mbiri yoyipa ya dzikolo anakanthidwa ndi mliri ndipo anafa pamaso pa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amuna amene anaipsa mbiri ya dziko, anafa ndi mliri pamaso pa Yehova.