Numbers 14:42 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musapite, kuti mungaphedwe pamaso pa adani anu, pakuti Chauta sali nanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musakwereko, pakuti Yehova sali pakati pa inu; kuti angakukantheni adani anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musapite chifukwa Yehova sali pakati panu. Mudzagonjetsedwa ndi adani anu
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musakwereko, pakuti Yehova sali pakati pa inu; kuti angakukantheni adani anu.