Numbers 15:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa buledi wanu woyamba, mudzaperekeko mmodzi kuti adzakhale nsembe. Mudzampereke monga momwe mumaperekera zopereka za popunthira tirigu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pa mtanda wanu woyamba muperekeko kamtanda, kakhale nsembe yokweza; monga mumachitira nsembe yokweza ya popuntha tirigu, momwemo muzikakweza,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa buledi wanu woyamba, mukapereke mmodzi monga nsembe, ngati chopereka chochokera ku malo wopunthira tirigu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pa mtanda wanu woyamba muperekeko kamtanda, kakhale nsembe yokweza; monga mumacitira nsembe yokweza ya popuntha tirigu, momwemo muzikakweza.