Numbers 16:31 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mose atangomaliza kulankhula mau ameneŵa, nthaka idang'ambika pamene padaali iwopo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atangotsiriza kuyankhula zimenezi, nthaka ya pamene anayimapo inagawikana
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali, pakutha iye kunena mau awa onse, nthaka inang'ambika pansi pao;