Numbers 18:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Iwowo adzakutumikirani ndi kugwiranso ntchito zonse zam'chihema. Koma asadzafike pafupi ndi zipangizo za m'malo opatulika kapena guwa, kuti iwowo pamodzi ndi inuyo mungafe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo asunge udikiro wako, ndi udikiro wa chihema chonse; koma asayandikize zipangizo za malo opatulika, ndi guwa la nsembe, kuti mungafe, iwo ndi inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwowo azikutumikirani ndipo azichita ntchito zonse za ku tenti, koma asamafike pafupi ndi zipangizo za ku malo opatulika kapena guwa lansembe, kuopa kuti iwo ndi inu mungafe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo asunge udikiro wako, ndi udikiro wa cihema conse; koma asayandikize zipangizo za malo opatulika, ndi guwa la nsembe, kuti mungafe, iwo ndi inu.