Numbers 20:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo adayamba kukangana ndi Mose, adati, “Kukadakhala bwino tikadafera pamodzi ndi abale athu aja amene adafa pamaso pa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anthu anatsutsana ndi Mose, nanena, nati, Mwenzi titangomwalira muja abale athu anamwalira pamaso pa Yehova!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anakangana ndi Mose kuti, “Kunali bwino ifenso tikanangofa pamene abale athu anafa pamaso pa Yehova!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anthu anatsutsana ndi Mose, nanena, nati, Mwenzi titangomwalira muja abale athu anamwalira pamaso pa Yehova!