Numbers 25:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero umuuze kuti ndikupangana naye tsopano chipangano chamtendere.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake nena, Taonani, ndimpatsa iye pangano langa la mtendere;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono muwuze kuti ndikhazikitsa pangano langa la mtendere ndi iye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace nena, Taonani, ndimpatsa iye pangano langa la mtendere;