Numbers 25:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho Aisraele adapembedza nao Baala wa ku Peori, ndipo Chauta adaŵapsera mtima Aisraele.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamene Israele anaphatikana ndi Baala-Peori, Yehova anapsa mtima pa Israele.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero Aisraeli anapembedza nawo Baala-Peori ndipo Yehova anawapsera mtima kwambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamene Israyeli anaphatikana ndi Baala Peori, Mulungu anapsa mtima pa Israyeli.