Numbers 27:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Inu Chauta, mwini mpweya wopatsa moyo anthu onse, musankhe munthu kuti aziyang'anira mpingowu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova, Mulungu wa mizimu ya anthu onse, aike munthu pa khamulo,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngati nʼkotheka Yehova, Mulungu wa mizimu ya anthu onse, sankhani munthu woti ayangʼanire gulu ili kuti
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova, Mulungu wa mizimu ya anthu onse, aike munthu pa khamulo,