Numbers 28:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chopereka cha chakumwa pa nkhosa iliyonse chikhale yokwanira lita limodzi. Muzithira vinyo waukaliyo m'malo opatulika, kuchipereka kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi nsembe yake yothira ya mwanawankhosa mmodziyo ndiyo limodzi la magawo anai la hini; m'malo opatulika uthirire Yehova nsembe yothira ya chakumwa cholimba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chopereka chachakumwa chikhale lita imodzi yachakumwa chaukali pa nkhosa iliyonse. Muzithira pamalo opatulika, kupereka kwa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi nsembe yace yothira ya mwana wa nkhosa mmodziyo ndiyo limodzi la magawo anai la bini; m'malo opatulika uthirire Yehova nsembe yothira ya cakumwa colimba.