Numbers 3:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo ana a Merari potsata mabanja ao ndi aŵa: Mali ndi Musi. Ameneŵa ndiwo mabanja a Levi potsata banja la makolo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi ana a Merari monga mwa mabanja ao: Mali ndi Musi. Awa ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ana a Merari potsata mabanja awo ndi awa: Mali ndi Musi. Amenewa ndiwo anali mabanja a Alevi monga mwa makolo awo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi ana a Merari monga mwa mabanja ao: Mali ndi Musi. Awa ndi mabanja a Alevi monga mwa nyumba za makolo ao.