Numbers 31:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ulipsire Amidiyani chifukwa cha zimene adachitira Aisraele, tsono pambuyo pake udzafa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Abwezereni chilango Amidiyani chifukwa cha ana a Israele; utatero udzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Uwabwezere zoyipa Amidiyani chifukwa cha zimene anachitira Aisraeli. Ukatha kuchita zimenezi, iwe udzamwalira.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Abwezereni cilango Amidyani cifukwa ca ana a Israyeli; utatero udzaitanidwa kumka kwa anthu a mtundu wako.