Numbers 31:23 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
zonse zimene sizingathe kupsa ndi moto, muziike pa moto, ndipo zidzayeretsedwa. Komabe ziyeretsedwenso ndi madzi oyeretsera, ndipo chilichonse chimene chingathe kupsa ndi moto, muchiviike m'madzi omwewo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
zonse zakulola moto, mupititse m'moto, ndipo zidzakhala zoyera; koma muziyeretsenso ndi madzi akusiyanitsa. Koma zonse zosalola moto, muzipititse m'madzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndi china chilichonse chimene sichingapse ndi moto muchidutsitse pa moto, ndipo chidzayeretsedwa. Komanso chiyeretsedwe ndi madzi oyeretsa. Ndipo chilichonse chimene chingapse ndi moto muchidutsitse mʼmadzimo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
zonse zakulola moto, mupititse m'moto, ndipo zidzakhala zoyera; koma muziyeretsenso ndi madzi akusiyanitsa. Koma zonse zosalola moto, muzipititse m'madzi.