Numbers 32:41 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yairi wa fuko la Manase adapita kukalanda midzi ina naitcha Havoti-Yairi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yairi mwana wa Manase ananka nalanda midzi yao, naitcha Havoti-Yairi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yairi, mwana wa Manase analanda midzi yambiri ya Giliyadi ndi kuyitcha kuti Havoti-Yairi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yairi mwana wa Manase anamka nalanda midzi yao, naicha Havoti Yairi. Ndipo Noba anamka nalanda Kenati, ndi miraga yace, naucha Noba, dzina lace.