Numbers 32:42 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Noba adapita kukalanda mzinda wa Kenati pamodzi ndi midzi yake, ndipo adautcha Noba, kutengera dzina lake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Noba ananka nalanda Kenati, ndi milaga yake, nautcha Noba, dzina lake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Noba analanda Kenati ndi midzi yozungulira ndi kuyitcha Noba, kutengera dzina la iye mwini.