Numbers 35:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo ngati munthu abaya mnzake chifukwa cha chidani, kapena amulasa ndi chida atamubisalira, mnzakeyo naafa,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo akampyoza momkwiyira, kapena kumponyera kanthu momlalira, kuti wafa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo ngati wina wake, chifukwa cha udani, aganiza zokankha munthu wina kapena kumuponyera chinthu china mwadala munthuyo nʼkufa,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo akampyoza momkwiyira, kapena kumponyera kanthu momlalira, kuti wafa;