Numbers 4:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma asaloŵe kukayang'ana zinthu zopatulika mpang'ono pomwe, kuti angafe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma asalowe kukaona zopatulikazo pozikulunga, kuti angafe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Akohati asalowe kukaona zinthu zopatulika, ngakhale kanthawi pangʼono, chifukwa akatero adzafa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma asalowe kukaona zopatulikazo pozikulunga, kuti angafe.