Numbers 4:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ndipo chiŵerengero chao chidakwanira 2,750 potsata mabanja ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
atawawerenga mwa mafuko awo, anali 2,750.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo owerengedwa ao monga mwa mabanja ao ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi awiri kudza makumi asanu.